Luke 7:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono mkulu wina wa gulu la asilikali achiroma 100 anali ndi wantchito amene ankamukonda kwambiri. Wantchitoyo ankadwala, ndipo anali pafupi kufa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kapolo wa kenturiyo, wokondedwa naye, anadwala, nafuna kutsirizika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kumeneko wantchito wa Kenturiyo, amene amamukhulupirira kwambiri, anadwala ndipo anali pafupi kufa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kapolo wa kenturiyo, wokondedwa naye, anadwala, nafuna kutsirizika.