Malachi 3:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ine ndine Chauta, wosasinthika. Nchifukwa chake inu zidzukulu za Yakobe simudaonongeke.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Ine Yehova sindisinthika, chifukwa chake inu ana a Yakobo simunathedwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ine ndine Yehova, ndipo sindisintha. Choncho inu zidzukulu za Yakobo, simunawonongedwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Ine Yehova sindisinthika, cifukwa cace inu ana a Yakobo simunathedwa.