Mark 10:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo ophunzira aja adazizwa koposa, nayamba kufunsana kuti, “Tsono nanga angathe kupulumuka ndani?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anadabwa, nanena kwa Iye, Ndipo angathe kupulumuka ndani?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ophunzira anadabwa kwambiri, ndipo anati kwa wina ndi mnzake, “Nanga ndani amene angapulumuke?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anadabwa, nanena kwa Iye, Ndipo angathe kupulumuka ndani?