Mark 10:41 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene khumi ena aja adamva zimenezi, adapsera mtima Yakobeyo ndi Yohaneyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene khumiwo anamva, anayamba kupsa mtima chifukwa cha Yakobo ndi Yohane.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ophunzira khumiwo otsalawo atamva izi anapsera mtima Yakobo ndi Yohane.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene khumiwo anamva, anayamba kupsa mtima cifukwa ca Yakobo ndi Yohane.