Mark 10:50 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pomwepo iye uja adadzambatuka, mwinjiro wake uko chi, kuthamangira kwa Yesu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iye anataya chofunda chake, nazunzuka, nadza kwa Yesu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anaponya mkanjo wake kumbali, analumpha nabwera kwa Yesu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iye anataya copfunda cace, nazunzuka, nadza kwa Yesu.