Mark 11:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ophunzirawo adaŵayankha monga momwe adaaŵauzira Yesu. Tsono anthuwo adaŵalola kuti ammasule.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anati kwa iwo monga momwe ananena Yesu: ndipo anawalola iwo apite naye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anayankha monga mmene Yesu anawawuzira, ndipo anthu aja anawalola kuti apite.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anati kwa iwo monga momwe ananena Yesu: ndipo anawalola iwo apite naye.