Mark 13:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adayamba kuŵauza kuti, “Chenjerani kuti wina aliyense asadzakusokezeni.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yesu anayamba kunena nao, Yang'anirani kuti munthu asakusocheretseni.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anawawuza kuti, “Chenjerani kuti wina asakunyengeni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yesu anayamba kunena nao, Yang'anirani kuti munthu asakusoceretseni.