Mark 14:33 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adatengako Petro, Yakobe ndi Yohane. Yesu adayamba kugwidwa ndi chisoni ndi kuvutika mu mtima.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anatenga pamodzi ndi Iye Petro, ndi Yakobo, ndi Yohane, nayamba kudabwa kwambiri, ndi kusauka mtima ndithu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anatenga Petro, Yakobo ndi Yohane, ndipo anayamba kumva chisoni kwambiri ndi kuvutika mu mtima.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anatenga pamodzi ndi Iye Petro, ndi Yakobo, ndi Yohane, nayamba kudabwa kwambiri, ndi kusauka mtima ndithu.