Mark 14:35 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adapita patsogolo pang'ono, nadzigwetsa pansi, nkuyamba kupemphera. Adati, “Ngati nkotheka nthaŵi yoopsa ino indipitirire.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Iye anapita m'tsogolo pang'ono, nagwa pansi, napemphera kuti ngati nkutheka nthawi imene impitirire.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atapita patsogolo pangʼono, anagwa pansi ndi kupemphera kuti ngati ndi kotheka oralo limupitirire.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Iye anapita m'tsogolo pang'ono, nagwa pansi, napemphera kuti ngati nkutheka nthawi imene impitirire.