Mark 14:48 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Yesu adaŵafunsa anthu aja kuti, “Bwanji mwachita kunditengera malupanga ndi zibonga, ngati kuti ndine chigaŵenga?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yesu anayankha nati kwa iwo, Kodi mwatuluka ndi malupanga ndi mikunkhu kundigwira Ine monga wachifwamba?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anati, “Kodi Ine ndikutsogolera gulu lowukira, kuti mubwera ndi malupanga ndi zibonga kudzandigwira?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yesu anayankha nati kwa iwo, Kodi mwaturuka ndi malupanga ndi mikunkhu kundigwira ine monga wacifwamba?