Mark 14:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Yesu adati, “Mlekeni maiyu, mukumuvutiranji kodi? Zimenetu wandichitira iyeyuzi nzabwino kwambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Yesu anati, Mlekeni, mumvutiranji? Wandichitira Ine ntchito yabwino.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anati, “Musiyeni, chifukwa chiyani mukumuvutitsa? Wandichitira Ine chinthu chabwino.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma Yesu anati, Mlekeni, mumbvutiranji? wandicitira Ine nchito yabwino.