Mark 14:69 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma mtsikana uja adamuwona, nayambanso kuuza amene anali pamenepo kuti, “Akulu ameneŵa anali m'gulu lomweli.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anamuona mdzakaziyo, nayambanso kunena ndi iwo akuimirirapo, Uyu ngwa awo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene mtsikana wantchitoyo anamuona iye, anatinso kwa iwo amene anayimirira pomwepo, “Munthu uyu ndi mmodzi mwa iwo.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anamuona mdzakaziyo, nayambanso kunena ndi iwo akuimirirapo, Uyu ngwa awo.