Mark 14:71 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Petro adayamba kudzitemberera nkumalumbira kuti, “Mtheradi, munthu amene mukunenayu ine sindimdziŵa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma iye anayamba kutemberera, ndi kulumbira, Sindimdziwa munthuyu mulikunena.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anayamba kudzitemberera, nalumbira kuti, “Sindimudziwa munthu ameneyu.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma iye anayamba kutemberera, ndi kulumbira, Sindimdziwa munthuyu mulikunena.