Mark 15:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ankamumenya m'mutu ndi ndodo, namamthira malovu, nkumamugwadira monyodola.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anampanda Iye pamutu pake ndi bango, namthira malovu, nampindira maondo, namlambira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo anamugogoda pa mutu mobwerezabwereza ndi ndodo ndi kumulavulira. Anamugwadira ndi kumulambira Iye.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anampanda Iye pamutu pace ndi bango, namthira malobvu, nampindira maondo, namlambira.