Mark 16:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngakhale atamva kuti Yesu ali moyo, ndipo kuti Maria wamuwona, iwo sadakhulupirire.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iwowo, pamene anamva kuti ali moyo, ndi kuti adapenyeka kwa iye, sanamvere.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atamva kuti Yesu ali moyo ndikuti amuona, iwo sanakhulupirire.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iwowo, pamene anamva kuti ali moyo, ndi kuti adapenyeka kwa iye, sanamvera.