Mark 16:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ankafunsana kuti, “Kodi ndani akatichotsere chimwala cha pakhomo pa manda chija?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo analikunena mwa okha, Adzatikunkhunizira ndani mwalawo, pakhomo la manda?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndipo anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Kodi akatikugudubuzira mwala pa khomo la manda ndani?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo analikunena mwa okha, Adzatikunkhunizira ndam mwalawo, pa khomo la manda?