Mark 3:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pambuyo pake Yesu adapita kwao, ndipo anthu ambiri adasonkhananso, kotero kuti Iye ndi ophunzira ake analibe ndi mpata womwe wodyera chakudya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anthu ambiri anasonkhananso, kotero kuti sanathe iwo konse kudya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pambuyo pake Yesu analowa mʼnyumba, ndipo gulu la anthu linasonkhananso, kotero kuti Iye pamodzi ndi ophunzira ake sanapeze mpata kuti adye.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anthu ambiri anasonkhananso, kotero kuti sanathe iwo konse kudya.