Mark 3:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu a mu ufumu uliwonse akayamba kuukirana, ufumuwo sungalimbe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ufumu ukagawanika pa uwu wokha, sukhoza kukhazikika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati ufumu ugawanikana mwa iwo okha, ufumu umenewo sungakhalitse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ufumu ukagawanika pa uwu wokha, sukhoza kukhazikika.