Mark 3:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono ngati a mu ufumu wa Satana aukirana okhaokha nagaŵikana, Satanayo sangalimbe, ndiye kuti watha basi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Satana akadziukira mwini yekha, nagawanika, sakhoza kukhazikika, koma atsirizika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo ngati Satana adzitsutsa yekha sangathe kuyima; ulamuliro wake watha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Satana akadziukira mwini yekha, nagawanika, sakhoza kukhazikika, koma atsirizika.