Mark 3:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adalankhula zimenezi poona kuti anthu aja ankanena kuti, “Wagwidwa ndi mzimu woipa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuti adanena, Ali ndi mzimu wonyansa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ananena izi chifukwa anati, “Ali ndi mzimu woyipa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pakuti adanena, Ali ndi mzimu wonyansa.