Mark 3:33 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Iye adati, “Amai anga! Abale anga! Otinso?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anawayankha nanena, Amai wanga ndi abale anga ndani?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anafunsa kuti, “Amayi ndi abale anga ndi ndani?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anawayankha nanena, Amai wanga ndi abale anga ndani?