Mark 4:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mbeu zofesedwa pa zitsamba za minga zija zikutanthauza anthu amene amaŵamva mau a Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ena ndiwo akufesedwa kuminga; iwo ndiwo amene adamva mau,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Komabe ena, monga mbewu zofesedwa pakati pa minga, amamva mawu;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ena ndiwo akufesedwa kuminga; iwo ndiwo amene adamva mau,