Mark 4:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma pamene dzuŵa lidakwera, zidapserera kenaka zidauma, chifukwa zinali zosazika mizu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo litakwera dzuwa zinapserera; ndipo popeza zinalibe mizu zinakhwinyata.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma dzuwa litakwera, mbewuzo zinapserera, ndipo zinawuma chifukwa zinalibe mizu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo litakwera dzuwa zinapserera; ndipo popeza zinalibe mizu zinakhwinyata.