Mark 5:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adaatero chifukwa Yesu anali atanena kuti, “Mzimu woipawe, tuluka mwa munthuyu!”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti ananena kwa iye, Tuluka iwe, mzimu wonyansa, kwa munthuyu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti Yesu anati kwa iye, “Tuluka mwa munthuyu, iwe mzimu woyipa!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti ananena kwa iye, Turuka iwe, mzimu wonyansa, kwa munthuyu.