Mark 6:44 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwa anthu amene adaadya bulediyo amuna okha adaalipo zikwi zisanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo amene anadya mikate iyo anali amuna zikwi zisanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chiwerengero cha amuna amene anadya chinali 5,000.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo amene anadya mikate iyo anali amuna zikwi zisanu.