Mark 7:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kenaka Yesu adati, “Inu mumasiya Malamulo a Mulungu, nkumasunga miyambo ya anthu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Musiya lamulo la Mulungu, nimusunga mwambo wa anthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwasiya malamulo a Mulungu ndipo mwagwiritsitsa miyambo ya anthu.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musiya lamulo la Mulungu, nimusunga mwambo wa anthu.