Mark 8:36 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nanga ndiye kuti munthu wapindulanji atapata zonse za pansi pano, iyeyo nkutaya moyo wake?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti munthu apindulanji akadzilemezera dziko lonse, natayapo moyo wake?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi munthu adzapindulanji akalandira dziko lonse lapansi, koma ndi kutaya moyo wake?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti munthu apindulanji akadzilemezera dziko lonse, natayapo moyo wace?