Mark 8:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu amene adaali pamenepo, amuna okha adaalipo ngati zikwi zinai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iwo anali ngati zikwi zinai; ndipo Iye analawirana nao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Panali amuna pafupifupi 4,000. Ndipo atawawuza kuti apite kwawo,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iwo anali ngati zikwi zinai; ndipo Iye analawirana nao.