Mark 9:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono adamufunsa kuti, “Nanga bwanji aphunzitsi a Malamulo amati Eliya adzayenera kuyamba wabwera?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anamfunsa Iye, nanena, Nanga alembi anena kuti adzayamba kufika Eliya?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo anamufunsa Iye kuti, “Nʼchifukwa chiyani aphunzitsi amalamulo amati Eliya ayenera kuyamba wabwera?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anamfunsa Iye, nanena, Nanga alembi anena kuti adzayamba kufika Eliya?