Mark 9:33 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu ndi ophunzira ake adafika ku Kapernao. Ataloŵa m'nyumba, Iye adaŵafunsa kuti, “Kodi panjira paja mumatsutsana zotani?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iwo anadza ku Kapernao; ndipo pamene anakhala m'nyumba, Iye anawafunsa, Munalikutsutsana ninji panjira?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anafika ku Kaperenawo. Pamene anali mʼnyumba, anawafunsa kuti, “Kodi mumatsutsana chiyani mʼnjira muja?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iwo anadza ku Kapernao; ndipo pamene anakhala m'nyumba, Iye anawafunsa, Munalikutsutsana ninji panjira?