Mark 9:36 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atatero adatenga mwana, namkhazika pakati pao nkumufungata, naŵauza kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anatenga kamwana, nakaika pakati pao, nakayangata, nanena nao,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anatenga kamwana nakayimiritsa pakati pawo ndipo anawawuza kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anatenga kamwana, nakaika pakati pao, nakayangata, nanena nao,