Mark 9:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono padafika mtambo, nuŵaphimba, ndipo mumtambomo mudamveka mau akuti, “Uyu ndiye Mwana wanga amene ndimamkonda, muzimumvera.”?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo panadza mtambo wakuwaphimba iwo; ndipo mau munatuluka m'mtambomo, kuti, Uyu ndiye Mwana wanga wokondedwa; mverani Iye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo mtambo unaoneka ndi kuwaphimba, ndipo mawu anamveka kuchokera mu mtambo kuti, “Uyu ndi Mwana wanga wokondedwa. Mvereni Iye!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo panadza mtambo wakuwaphimba iwo; ndipo mau munaturuka m'mtambomo, kuti, Uyu ndiye Mwana wanga wokondedwa; mverani Iye.