Mark 9:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwadzidzidzi ophunzirawo poyang'anayang'ana, adangoona kuti palibenso wina amene anali nawo pamenepo, koma Yesu yekha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo dzidzidzi pounguzaunguza, sanapenye munthu wina yense, koma Yesu yekha, ndi iwo eni.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwadzidzidzi, atayangʼanayangʼana, sanaonenso wina aliyense ali ndi iwo kupatula Yesu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo dzidzidzi pounguzaunguza, sanapenya munthu wina yense, koma Yesu yekha, ndi iwo eni.