Matthew 1:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
koma sadamdziŵe mpaka adabala mwana wamwamuna. Pambuyo pake Yosefe adatcha mwanayo dzina loti Yesu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo sanamdziwe iye kufikira atabala mwana wake; namutcha dzina lake Yesu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma sanagone malo amodzi mpaka mwanayo atabadwa ndipo anamutcha dzina lake Yesu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo sanamdziwa iye kufikira atabala rriwana wace; namucha dzina lace Yesu.