Matthew 10:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Poloŵa m'nyumba, muzikanena kuti, ‘Mtendere ukhale ndi inu’.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo polowa m'nyumba muwalonjere.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene mulowa mʼnyumba mupereke moni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo polowa m'nyumba muwalankhule.