Matthew 10:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pajatu odzalankhula si ndinu ai, koma Mzimu wa Atate anu ndiye amene adzalankhula kudzera mwa inu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuti wolankhula si ndinu, koma Mzimu wa Atate wanu akulankhula mwa inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
pakuti sindinu mudzanena, koma Mzimu Woyera wa Atate anu, adzayankhula mwa inu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pakuti wolankhula si ndinu, koma Mzimu wa Atate wanu akulankhula mwa inu.