Matthew 10:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pitani, muzikalalika kuti, ‘Mulungu ali pafupi kukhazikitsa ufumu wake tsopano.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene mulikupita lalikani kuti, Ufumu wa Kumwamba wayandikira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene mukupita, muzikalalikira uthenga uwu: ‘Ufumu wakumwamba wayandikira.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene mulikupita lalikani kuti, Ufumu wa Kumwamba wayandikira.