Matthew 11:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo ngati mukufunadi kukhulupirira zimenezi, Yohaneyo ndiye Eliya uja ankati adzabwerayu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ngati mufuna kulandira, uyu ndiye Eliya amene amati akudza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo ngati inu mufuna kulandira izi, iyeyu ndi Eliya amene ankanena kuti adzabwera uja.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ngati mufuna kulandira, uyu ndiye Eliya amene amati akudza.