Matthew 11:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi Inu ndinu uja ankati adzabwerayu, kapena tiziyembekezera wina?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nati kwa Iye, Inu ndinu wakudza kodi, kapena tiyembekezere wina?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anamufunsa kuti, “Kodi Inu ndinu uja ankanena kuti mudzabwerayu kapena tidikire wina?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
nati kwa Iye, Inu ndinu wakudza kodi, kapena tiyembekezere wina?