Matthew 12:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Nayu mtumiki wanga amene ndamsankha. Ndimamkonda, ndipo mtima wanga umasangalala naye kwambiri. Ndidzaika Mzimu wanga mwa iyeyo, ndipo adzalalika za chilungamo kwa anthu a mitundu ina.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taona mnyamata wanga, amene ndinamsankha, wokondedwa wanga, amene moyo wanga ukondwera naye; pa Iye ndidzaika Mzimu wanga, ndipo Iye adzalalikira chiweruzo kwa akunja.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Taonani mnyamata wanga amene ndinamusankha, Wokondedwa wanga, amene moyo wanga ukondwera naye. Pa Iye ndidzayika Mzimu wanga, ndipo Iye adzalalikira chiweruzo kwa akunja.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taona mnyamata wanga, amene ndinamsankha, Wokondedwa wanga, amene moyo wanga ukondwera naye; Pa Iye ndidzaika Mzimu wanga, Ndipo Iye adzalalikira ciweruzo kwa akunja.