Matthew 13:50 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
nkumaŵaponya m'ng'anjo ya moto. Kumeneko adzalira ndi kukukuta mano.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nadzawataya m'ng'anjo yamoto; komweko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo oyipa adzawaponya mʼngʼanjo ya moto kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
nadzawataya m'ng'anjo yamoto; komweko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.