Matthew 13:51 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adaŵafunsa anthu aja kuti, “Mwazimvetsa zonsezi kodi?” Iwo adati, “Inde.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwamvetsa zonsezi kodi? Iwo anati kwa Iye, Inde.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anawafunsa kuti, “Kodi mwamvetsetsa zonsezi?” Iwo anayankha kuti, “Inde.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwamvetsa zonsezi kodi? lwo anati kwa Iye, inde.