Matthew 13:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma pamene dzuŵa lidakwera, zidapserera kenaka zidauma, chifukwa zinali zosazika mizu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo popeza zinalibe mizu zinafota.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma dzuwa litakwera, mbewu zinapserera ndipo zinawuma chifukwa zinalibe mizu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo popeza zinalibe mizu zinafota.