Matthew 14:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma tsono anthu amene adaadyawo analipo ngati zikwi zisanu amuna okha, osaŵerenga akazi ndi ana.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anadyawo anali amuna monga zikwi zisanu, kuwaleka akazi ndi ana.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chiwerengero cha amene anadya kupatulako amayi ndi ana chinali pafupifupi amuna 5,000.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anadyawo anali amuna monga zikwi zisanu, kuwaleka akazi ndi ana.