Matthew 14:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adati, “Chabwino, bwera.” Tsono Petro adatuluka m'chombo nayamba kuyenda pa madzi kupita kwa Yesu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Iye anati, Idza. Ndipo Petro anatsika m'ngalawa, nayenda pamadzi, kufika kwa Yesu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anati, “Bwera.” Pamenepo Petro anatuluka mʼbwato ndipo anayenda pa madzi kupita kwa Yesu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Iye anati, Idza, Ndipo Petro anatsika m'ngalawa, nayenda pamadzi, kufika kwa Yesu.