Matthew 14:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakuti Yohane adaauza Herode kuti, “Nkulakwira Malamulo kumukwatira mkaziyo.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Yohane ananena kwa iye, Sikuloledwa kwa iwe kukhala naye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chifukwa Yohane anakhala akunena kwa iye kuti, “Sichololedwa kwa inu kutenga mkaziyo.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Yohane ananena kwa iye, Sikuloledwa kwa iwe kukhala naye.