Matthew 14:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kwenikweni Herode ankafuna kupha Yohane, koma ankaopa anthu, chifukwa iwo ankati ndi mneneri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pofuna kumupha iye, anaopa khamu la anthu, popeza anamuyesa iye mneneri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Herode anafuna kupha Yohane koma iye anaopa anthu chifukwa anamuyesa iye mneneri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pofuna kumupha iye, anaopa khamu la anthu, popeza anamuyesa iye mneneri.