Matthew 15:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma zotuluka m'kamwa mwa munthu zimachokera mu mtima, ndipo zimenezi ndizo zimamuipitsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma zakutuluka m'kamwa zichokera mumtima; ndizo ziipitsa munthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma zinthu zimene zituluka mʼkamwa zimachokera mu mtima ndipo zimenezi zimamuchititsa munthu kukhala woyipa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma zakuturuka m'kamwa zicokera mumtima; ndizo ziipitsa munthu.