Matthew 15:38 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma tsono anthu amene adaadyawo, analipo zikwi zinai amuna okha, osaŵerenga akazi ndi ana.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anadyawo anali amuna zikwi zinai kuwaleka akazi ndi ana.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chiwerengero cha anthu amene anadya chinali 4,000 kupatula amayi ndi ana.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anadyawo anali amuna zikwi zinai kuwaleka akazi ndi ana.