Matthew 15:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“ ‘Anthu aŵa amangondilemekeza ndi pakamwa chabe, koma mtima wao uli kutali ndi Ine.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anthu awa andilemekeza Ine ndi milomo yao; koma mtima wao uli kutali ndi Ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“ ‘Anthu awa amandilemekeza Ine ndi milomo yawo, koma mitima yawo ili kutali ndi Ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anthu awa andilemekeza Ine ndi milomo yao; Koma mtima wao uli kutari ndi Ine.